1 Mbiri 5:11 - Buku Lopatulika11 Ndi ana a Gadi anakhala pandunji pao m'dziko la Basani mpaka Saleka: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndi ana a Gadi anakhala pandunji pao m'dziko la Basani mpaka Saleka: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ana a Gadi adakhala kumpoto kwa Arubeni m'dziko la Basani mpaka kukafika ndithu kuvuma ku Saleka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Anthu a fuko la Gadi anakhala moyandikana ndi fuko la Rubeni ku Basani mpaka ku Saleka: Onani mutuwo |