1 Mbiri 5:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo ana a Rubeni mwana woyamba wa Israele, (pakuti ndiye mwana woyamba; koma popeza anaipsa kama wa atate wake ukulu wake unapatsidwa kwa ana a Yosefe mwana wa Israele, koma m'buku la chibadwidwe asayesedwe monga mwa ukulu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo ana a Rubeni mwana woyamba wa Israele, (pakuti ndiye mwana woyamba; koma popeza anaipsa kama wa atate wake ukulu wake unapatsidwa kwa ana a Yosefe mwana wa Israele, koma m'buku la chibadwidwe asayesedwe monga mwa ukulu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Naŵa ana a Rubeni, mwana wachisamba wa Israele. Inde Rubeni analidi mwana wachisamba, koma chifukwa adaagona ndi mkazi wina wamng'ono wa bambo wake, uchisamba wakewo udapatsidwa kwa Yosefe, mng'ono wake. Motero Rubeniyo saoneka pa mndandanda wa maina potsata za kubadwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ana a Rubeni mwana woyamba wa Israeli (iye anali woyamba kubadwa, koma atagona ndi mkazi wamngʼono wa abambo ake, ulemu wake wokhala mwana woyamba unaperekedwa kwa ana a Yosefe. Kotero iye sanalembedwe pa mndandanda wa mayina ngati mwana woyamba kubadwa, Onani mutuwo |