Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 4:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Hakozi anabala Anubu, ndi Zobeba, ndi mabanja a Ahariyele mwana wa Harumu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Hakozi anabala Anubu, ndi Zobeba, ndi mabanja a Ahariyele mwana wa Harumu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Kozi adabereka Anubu, Zobeba, ndi mabanja a Ahariyele, mwana wa Harumu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 ndi Kozi, amene anali abambo ake a Anubi ndi Hazo-Beba ndi mabanja a Ahariheli mwana wa Harumi.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 4:8
4 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Hela ndiwo Zereti, Izihara, ndi Etinani.


Ndipo Yabezi analemekezedwa koposa abale ake; ndi make anamutcha dzina lake Yabezi, ndi kuti, Popeza ndambala mwaululu.


Ndi ana a ansembe: ana a Habaya, ana a Hakozi, ana a Barizilai, amene anadzitengera mkazi wa ana aakazi a Barizilai Mgiliyadi, natchedwa dzina lao.


Potsatizana naye Meremoti mwana wa Uriya mwana wa Hakozi anakonza gawo lina, kuyambira kukhomo la nyumba ya Eliyasibu kufikira malekezero ake a nyumba ya Eliyasibu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa