Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 4:6 - Buku Lopatulika

6 Ndi Naara anambalira Ahuzamu, ndi Hefere, ndi Temeni, ndi Haahasitari. Iwo ndiwo ana a Naara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndi Naara anambalira Ahuzamu, ndi Hefere, ndi Temeni, ndi Haahasitari. Iwo ndiwo ana a Naara.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Nara adamubalira Ahuzamu, Hefere, Temeni, ndi Haahasitari. Ameneŵa ndiwo anali ana a Nara.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Naara anamuberekera Ahuzamu, Heferi, Temani ndi Haahasitari. Awa ndiwo anali ana a Naara.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 4:6
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Asiriya atate wa Tekowa anali nao akazi awiri: Hela, ndi Naara.


Ndi ana a Hela ndiwo Zereti, Izihara, ndi Etinani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa