1 Mbiri 3:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo ombadwira mu Yerusalemu ndi awa: Simea, ndi Sobabu, ndi Natani, ndi Solomoni, anai a Batisuwa mwana wamkazi wa Amiyele; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo ombadwira m'Yerusalemu ndi awa: Simea, ndi Sobabu, ndi Natani, ndi Solomoni, anai a Batisuwa mwana wamkazi wa Amiyele; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ana amene adabadwira ku Yerusalemu ndi aŵa: Simea, Sobabu, Natani ndi Solomoni. Ameneŵa ndiwo ana anai amene adamubalira Batisuwa mwana wa Amiyele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 ndipo ana amene anabadwira ku Yerusalemuko anali awa: Samua, Sobabu, Natani ndi Solomoni. Ana anayi awa anali a Batisuwa mwana wa Amieli. Onani mutuwo |