Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 3:16 - Buku Lopatulika

16 Ndi ana a Yehoyakimu: Yekoniya mwana wake, Zedekiya mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndi ana a Yehoyakimu: Yekoniya mwana wake, Zedekiya mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Ana aamuna a Yehoyakimu anali aŵa: Yekoniya ndi Zedekiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Ana a Yehoyakimu: Yekoniya ndi Zedekiya mwana wake.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 3:16
12 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu ya Babiloni analonga Mataniya mbale wa atate wake akhale mfumu m'malo mwake, nasanduliza dzina lake likhale Zedekiya.


Nagona Yehoyakimu ndi makolo ake, ndipo Yehoyakini mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Yehoyakini anali wa zaka khumi mphambu zisanu ndi zitatu polowa iye ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu miyezi itatu; ndi dzina la make ndiye Nehusita mwana wa Elinatani wa ku Yerusalemu.


Ndipo kunali chaka cha makumi atatu mphambu zisanu ndi ziwiri cha kumtenga ndende Yehoyakini mfumu ya Yuda, mwezi wakhumi ndi ziwiri, tsiku la makumi awiri mphambu asanu ndi awiri la mwezi, Evili-Merodaki mfumu ya Babiloni anamuweramutsa mutu wake wa Yehoyakini mfumu ya Yuda atuluke m'kaidi, chaka cholowa iye ufumu wake;


Ndi ana a Yosiya: woyamba Yohanani, wachiwiri Yehoyakimu, wachitatu Zedekiya, wachinai Salumu.


Ndi mwana wa Yekoniya: Asiri, Sealatiele mwana wake,


Ndipo Yehova Mulungu wa makolo ao anatumiza kwa iwo ndi dzanja la mithenga yake, nalawirira mamawa kuituma, chifukwa anamvera chifundo anthu ake, ndi pokhala pake;


Yehoyakini anali wa zaka zisanu ndi zitatu polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu miyezi itatu, ndi masiku khumi; nachita choipa pamaso pa Yehova.


Pali Ine, ati Yehova, ngakhale Koniya mwana wake wa Yehoyakimu mfumu ya Yuda akadakhala mphete ya padzanja langa lamanja, ndikadachotsa iwe kumeneko;


Kodi munthu uyu Koniya ndiye mbiya yopepuka yosweka? Kodi ndiye mbiya yosakondweretsa? Chifukwa chanji atulutsidwa iye, ndi mbeu zake, ndi kuponyedwa m'dziko limene salidziwa?


Ndipo Zedekiya mwana wa Yosiya anakhala mfumu m'malo a Koniya mwana wa Yehoyakimu, amene Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni inamlowetsa mfumu m'dziko la Yuda.


ndi Yosiya anabala Yekoniya ndi abale ake pa nthawi yakutengedwa kunka ku Babiloni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa