1 Mbiri 3:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo mwana wa Solomoni ndiye Rehobowamu, Abiya mwana wake, Asa mwana wake, Yehosafati mwana wake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo mwana wa Solomoni ndiye Rehobowamu, Abiya mwana wake, Asa mwana wake, Yehosafati mwana wake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Nazi zidzukulu za Solomoni: Rehobowamu adabereka Abiya, Abiya adabereka Asa, Asa adabereka Yehosafati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mwana wa Solomoni anali Rehabiamu, Rehabiamu anabereka Abiya, Abiya anabereka Asa, Asa anabereka Yehosafati, Onani mutuwo |