Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 27:4 - Buku Lopatulika

4 Woyang'anira chigawo cha mwezi wachiwiri ndiye Dodai Mwahohi ndi chigawo chake; ndi Mikiloti mtsogoleri, ndi m'chigawo chake munali zikwi makumi awiri mphambu zinai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Woyang'anira chigawo cha mwezi wachiwiri ndiye Dodai Mwahohi ndi chigawo chake; ndi Mikiloti mtsogoleri, ndi m'chigawo chake munali zikwi makumi awiri mphambu zinai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Dodai Mwahohi anali woyang'anira gulu la mwezi wachiŵiri. Mtsogoleri wa gulu limeneli anali Mikiloti. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Amene amalamulira gulu lachiwiri pa mwezi wachiwiri anali Dodai Mwahohi; Mikiloti ndiye anali mtsogoleri wa gulu lake. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 27:4
4 Mawu Ofanana  

Ndipo wotsatana naye Eleazara mwana wa Dodo mwana wa Mwahohi, mmodzi wa ngwazi zitatu zokhala ndi Davide pamene iwo anatonza Afilisti osonkhanidwa kunkhondo kumeneko, atachoka Aisraele;


Ndi pambuyo pake Eleazara mwana wa Dodo Mwahohi, ndiye mmodzi wa atatu aja amphamvu.


Ndiye wa ana a Perezi, mkulu wa akazembe onse a khamu mwezi woyamba.


Kazembe wachitatu wa khamu wa mwezi wachitatu ndiye Benaya mwana wa Yehoyada wansembe wamkulu; ndi m'chigawo mwake munalinso zikwi makumi awiri mphambu zinai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa