Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 27:3 - Buku Lopatulika

3 Ndiye wa ana a Perezi, mkulu wa akazembe onse a khamu mwezi woyamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndiye wa ana a Perezi, mkulu wa akazembe onse a khamu mwezi woyamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Iyeyu anali mdzukulu wa Perezi, ndipo ndiye anali mkulu wa atsogoleri onse ankhondo mwezi woyamba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Iyeyu anali chidzukulu cha Perezi ndipo anali mkulu wa atsogoleri onse a ankhondo mwezi woyamba.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 27:3
7 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene iye anabweza dzanja lake, kuti, taona, mbale wake anabadwa, ndipo namwino anati, Wadziphothyolera wekha bwanji? Chifukwa chake dzina lake linatchedwa Perezi.


Woyang'anira chigawo choyamba cha mwezi, woyamba ndiye Yasobeamu mwana wa Zabidiele; m'chigawo mwake munali zikwi makumi awiri mphambu zinai.


Woyang'anira chigawo cha mwezi wachiwiri ndiye Dodai Mwahohi ndi chigawo chake; ndi Mikiloti mtsogoleri, ndi m'chigawo chake munali zikwi makumi awiri mphambu zinai.


Ndipo anayamba kuyenda ambendera ya chigono cha ana a Yuda monga mwa magulu ao; woyang'anira gulu lake ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndipo ana a Yuda monga mwa mabanja ao ndiwo: Sela, ndiye kholo la banja la Asela; Perezi, ndiye kholo la banja la Aperezi; Zera, ndiye kholo la banja la Azera.


Wakubwera nacho chopereka chake tsiku loyamba ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu, wa fuko la Yuda:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa