1 Mbiri 27:3 - Buku Lopatulika3 Ndiye wa ana a Perezi, mkulu wa akazembe onse a khamu mwezi woyamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndiye wa ana a Perezi, mkulu wa akazembe onse a khamu mwezi woyamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Iyeyu anali mdzukulu wa Perezi, ndipo ndiye anali mkulu wa atsogoleri onse ankhondo mwezi woyamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iyeyu anali chidzukulu cha Perezi ndipo anali mkulu wa atsogoleri onse a ankhondo mwezi woyamba. Onani mutuwo |