Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 27:2 - Buku Lopatulika

2 Woyang'anira chigawo choyamba cha mwezi, woyamba ndiye Yasobeamu mwana wa Zabidiele; m'chigawo mwake munali zikwi makumi awiri mphambu zinai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Woyang'anira chigawo choyamba cha mwezi, woyamba ndiye Yasobeamu mwana wa Zabidiele; m'chigawo mwake munali zikwi makumi awiri mphambu zinai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Yosobeamu mwana wa Zabidiele ankayang'anira gulu loyamba pa mwezi woyamba. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Amene amalamulira gulu loyamba pa mwezi woyamba anali Yasobeamu mwana wa Zabidieli. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 27:2
4 Mawu Ofanana  

Maina a ngwazi Davide anali nazo ndiwo: Yosebu-Basebeti Mtakemoni, mkulu wa akazembe; ameneyu ndiye Adino Mwezni wolimbana ndi mazana atatu ophedwa nthawi imodzi.


Kuwerenga kwa amphamvu aja Davide anali nao ndi uku: Yasobeamu mwana wa Muhakimoni, mkulu wa makumi atatu aja, anasamulira mazana atatu mkondo wake, nawapha nthawi imodzi.


Ndipo ana a Israele monga mwa chiwerengo chao, kunena za akulu a nyumba za makolo ao, ndi akazembe a zikwi, ndi a mazana, ndi akapitao ao akutumikira mfumu mu ntchito iliyonse ya magawidwe, akulowa ndi kutuluka mwezi ndi mwezi, miyezi yonse ya chaka, chigawo chilichonse ncha amuna zikwi makumi awiri mphambu zinai.


Ndiye wa ana a Perezi, mkulu wa akazembe onse a khamu mwezi woyamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa