Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 26:9 - Buku Lopatulika

9 Ndi Meselemiya anali ndi ana, ndi abale odziwa mphamvu khumi mphambu asanu ndi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndi Meselemiya anali ndi ana, ndi abale odziwa mphamvu khumi mphambu asanu ndi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Kuchokera ku banja la Meselemiya kudasankhidwa anthu aluso 18.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Meselemiya anali ndi ana ndi abale ake amene anali aluso ndipo onse analipo 18.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 26:9
4 Mawu Ofanana  

A magawidwe a odikira a Akora: Meselemiya mwana wa Kore wa ana a Asafu.


Hosa yemwe wa ana a Merari anali ndi ana, wamkulu ndi Simiri; pakuti ngakhale sanali wobadwa woyamba, atate wake anamuyesa wamkulu;


Ndi maere a kum'mawa anagwera Selemiya. Ndipo anachitira maere Zekariya mwana wake, phungu wanzeru, ndi maere anamgwera kumpoto;


Onsewa ndiwo a ana a Obededomu; iwo ndi ana ao, ndi abale ao, anthu odziwa mphamvu yakutumikira, makumi asanu ndi limodzi mphambu awiri a Obededomu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa