Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 26:7 - Buku Lopatulika

7 Ana a Semaya: Otini, ndi Refaele, ndi Obedi, Elizabadi, amene abale ao ndiwo odziwa mphamvu, Elihu, ndi Semakiya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ana a Semaya: Otini, ndi Refaele, ndi Obedi, Elizabadi, amene abale ao ndiwo odziwa mphamvu, Elihu, ndi Semakiya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ana a Semaya naŵa: Otini, Refaele, Obede ndi Elizabadi amene anali ndi abale ao amphamvu, Elihu ndi Semakiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Ana a Semaya anali: Otini, Refaeli, Obedi ndi Elizabadi; abale ake, Elihu ndi Semakiya, analinso anthu amphamvu.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 26:7
3 Mawu Ofanana  

Kwa Semaya mwana wake yemwe kunabadwa ana, akulamulira nyumba ya atate wao; pakuti anali ngwazi zamphamvu.


Onsewa ndiwo a ana a Obededomu; iwo ndi ana ao, ndi abale ao, anthu odziwa mphamvu yakutumikira, makumi asanu ndi limodzi mphambu awiri a Obededomu.


Ndipo Salumu mwana wa Kore, mwana wa Ebiyasafu, mwana wa Kora, ndi abale ake a nyumba ya atate wake; Akora anayang'anira ntchito ya utumiki, osunga zipata za Kachisi monga makolo ao; anakhala m'chigono cha Yehova osunga polowera;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa