1 Mbiri 26:6 - Buku Lopatulika6 Kwa Semaya mwana wake yemwe kunabadwa ana, akulamulira nyumba ya atate wao; pakuti anali ngwazi zamphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Kwa Semaya mwana wake yemwe kunabadwa ana, akulamulira nyumba ya atate wao; pakuti anali ngwazi zamphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Semaya mwana wake nayenso anali ndi ana amene anali otchuka m'mabanja a makolo ao, makamaka aŵiri omariza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mwana wake Semaya analinso ndi ana amene anali atsogoleri mʼbanja la abambo awo chifukwa anali anthu amphamvu. Onani mutuwo |