1 Mbiri 26:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Obededomu anali nao ana, woyamba Semaya, wachiwiri Yehozabadi, wachitatu Yowa, wachinai Sakara, wachisanu Netanele, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Obededomu anali nao ana, woyamba Semaya, wachiwiri Yehozabadi, wachitatu Yowa, wachinai Sakara, wachisanu Netanele, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Obededomu Mulungu anali ndi ana aŵa: wachisamba anali Semaya, wachiŵiri Yehozabadi, wachitatu Yowa, wachinai Sakara, wachisanu Netanele, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Obedi-Edomu analinso ndi ana awa: woyamba Semaya, wachiwiri Yehozabadi, wachitatu Yowa, wachinayi Sakara, wachisanu Netaneli, Onani mutuwo |