Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 26:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo Meselemiya anali ndi ana, woyamba Zekariya, wachiwiri Yediyaele, wachitatu Zebadiya, wachinai Yatiniele,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo Meselemiya anali ndi ana, woyamba Zekariya, wachiwiri Yediyaele, wachitatu Zebadiya, wachinai Yatiniele,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Meselemiya anali ndi ana aŵa: wachisamba anali Zekariya, wachiŵiri Yediyale, wachitatu Zebadiya, wachinai Yatiniele,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Meselemiya anali ndi ana awa: woyamba Zekariya, wachiwiri Yediaeli, wachitatu Zebadiya, wachinayi Yatinieli,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 26:2
3 Mawu Ofanana  

A magawidwe a odikira a Akora: Meselemiya mwana wa Kore wa ana a Asafu.


wachisanu Elamu, wachisanu ndi chimodzi Yehohanani, wachisanu ndi chiwiri Eliehoenai.


Zekariya mwana wa Meselemiya anali wodikira pakhomo pa chihema chokomanako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa