Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 26:14 - Buku Lopatulika

14 Ndi maere a kum'mawa anagwera Selemiya. Ndipo anachitira maere Zekariya mwana wake, phungu wanzeru, ndi maere anamgwera kumpoto;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndi maere a kum'mawa anagwera Selemiya. Ndipo anachitira maere Zekariya mwana wake, phungu wanzeru, ndi maere anamgwera kumpoto;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Selemiya adamsankha kuti azilonda pa khomo lakuvuma. Mwana wake Zekariya, phungu wanzeru, adamsankha kuti azilonda khomo lakumpoto.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Maere a chipata chakummwa anagwera Selemiya. Maere anachitikanso chifukwa cha mwana wake Zekariya, phungu wanzeru ndipo maere a chipata chakumpoto anagwera iye.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 26:14
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anachita maere, ang'ono ndi akulu, monga mwa nyumba za makolo ao, kuchitira zipata zonse.


Obededomu kumwera, ndi ana ake nyumba ya akatundu.


Ndi Meselemiya anali ndi ana, ndi abale odziwa mphamvu khumi mphambu asanu ndi atatu.


Zekariya mwana wa Meselemiya anali wodikira pakhomo pa chihema chokomanako.


Pa mbali zinai panali odikira kum'mawa, kumadzulo, kumpoto, ndi kumwera.


Ndipo Kore mwana wa Imina Mlevi, wa kuchipata cha kum'mawa, anayang'anira zopereka zaufulu za Mulungu, kugawira nsembe zokweza za Yehova, ndi zopatulika kwambiri.


Pamenepo ndinatumiza munthu kuitana Eliyezere, Ariyele, Semaya, ndi Elinatani, ndi Yaribu, ndi Elinatani, ndi Natani, ndi Zekariya, ndi Mesulamu, ndiwo akulu; ndi Yoyaribu ndi Elinatani, ndiwo aphunzitsi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa