Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 26:11 - Buku Lopatulika

11 wachiwiri Hilikiya, wachitatu Tebaliya, wachinai Zekariya; ana ndi abale onse a Hosa ndiwo khumi ndi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 wachiwiri Hilikiya, wachitatu Tebaliya, wachinai Zekariya; ana ndi abale onse a Hosa ndiwo khumi ndi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Wachiŵiri Hilikiya, wachitatu Tebaliya, wachinai anali Zekariya. Onse a m'banja la Hosa amene anali alonda analipo 13.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 wachiwiri Hilikiya, wachitatu Tebaliya ndipo wachinayi Zekariya. Ana ndi abale onse a Hosa analipo 13.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 26:11
3 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene adaitana mfumu, anawatulukira Eliyakimu mwana wa Hilikiya woyang'anira nyumba ya mfumu, ndi Sebina mlembi, ndi Yowa mwana wa Asafu wolemba mbiri.


Hosa yemwe wa ana a Merari anali ndi ana, wamkulu ndi Simiri; pakuti ngakhale sanali wobadwa woyamba, atate wake anamuyesa wamkulu;


Mwa iwowa munali magawidwe a odikira, mwa akulu a amuna akuchita udikiro wao, monga abale ao, kutumikira m'nyumba ya Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa