Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 26:10 - Buku Lopatulika

10 Hosa yemwe wa ana a Merari anali ndi ana, wamkulu ndi Simiri; pakuti ngakhale sanali wobadwa woyamba, atate wake anamuyesa wamkulu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Hosa yemwe wa ana a Merari anali ndi ana, wamkulu ndi Simiri; pakuti ngakhale sanali wobadwa woyamba, atate wake anamuyesa wamkulu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Kuchokera ku banja la Merari kudasankhidwa Hosa amene anali ndi ana aŵa: Simiri mtsogoleri (iyeyu ngakhale sanali mwana wachisamba, atate ake adaamsankhula kuti akhale mtsogoleri.)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Hosa Mmerari anali ndi ana awa: woyamba anali Simiri (ngakhale kuti iye sanali woyamba kubadwa, abambo ake anamusankha kuti akhale mtsogoleri),

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 26:10
4 Mawu Ofanana  

ndi Obededomu, ndi abale ake makumi asanu ndi limodzi mphambu asanu ndi atatu; ndi Obededomu mwana wa Yedutuni ndi Hosa akhale odikira;


wachiwiri Hilikiya, wachitatu Tebaliya, wachinai Zekariya; ana ndi abale onse a Hosa ndiwo khumi ndi atatu.


Ndi Meselemiya anali ndi ana, ndi abale odziwa mphamvu khumi mphambu asanu ndi atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa