1 Mbiri 26:1 - Buku Lopatulika1 A magawidwe a odikira a Akora: Meselemiya mwana wa Kore wa ana a Asafu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 A magawidwe a odikira a Akora: Meselemiya mwana wa Kore wa ana a Asafu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Magulu a alonda odikira pa khomo naŵa: m'gulu la Akora munali Meselemiya, mwana wa Kore, mmodzi mwa ana a Asafu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Magulu a alonda a pa zipata: Kuchokera ku banja la Kora: Meselemiya mwana wa Kore, mmodzi mwa ana a Asafu. Onani mutuwo |
Ndipo anaika monga mwa chiweruzo cha Davide atate wake zigawo za ansembe ku utumiki wao, ndi Alevi ku udikiro wao, kulemekeza Mulungu, ndi kutumikira pamaso pa ansembe, monga munayenera tsiku ndi tsiku; odikira omwe monga mwa zigawo zao ku chipata chilichonse; pakuti momwemo Davide munthu wa Mulungu adamuuza.