1 Mbiri 24:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo magawidwe a ana a Aroni ndi awa. Ana a Aroni: Nadabu, ndi Abihu, Eleazara, ndi Itamara. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo magawidwe a ana a Aroni ndi awa. Ana a Aroni: Nadabu, ndi Abihu, Eleazara, ndi Itamara. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Zidzukulu za Aroni ndi izi. Ana a Aroni naŵa: Nadabu, Abihu, Eleazara ndi Itamara. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Magulu a ana a Aaroni anali awa: Ana a Aaroni anali Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara. Onani mutuwo |
Ndipo anaika monga mwa chiweruzo cha Davide atate wake zigawo za ansembe ku utumiki wao, ndi Alevi ku udikiro wao, kulemekeza Mulungu, ndi kutumikira pamaso pa ansembe, monga munayenera tsiku ndi tsiku; odikira omwe monga mwa zigawo zao ku chipata chilichonse; pakuti momwemo Davide munthu wa Mulungu adamuuza.