Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 23:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo anawerengedwa Alevi oyambira zaka makumi atatu ndi mphambu, ndipo chiwerengo chao kuwawerenga mmodzimmodzi ndicho amuna zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo anawerengedwa Alevi oyambira zaka makumi atatu ndi mphambu, ndipo chiwerengo chao kuwawerenga mmodzimmodzi ndicho amuna zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Adaŵerenga Aleviwo kuyambira a zaka makumi atatu ndi kupitirirapo. Chiŵerengero chao chinali anthu 38,000.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Anawerenga Alevi kuyambira a zaka makumi atatu ndi kupitirirapo, ndipo chiwerengero cha amuna onse chinali 38,000.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 23:3
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anasonkhanitsa akulu onse a Israele, ndi ansembe ndi Alevi.


Awa ndi ana a Levi monga mwa nyumba za makolo ao, ndiwo akulu a nyumba za makolo a iwo owerengedwa mwa chiwerengero cha maina mmodzimmodzi, akugwira ntchito ya utumiki wa nyumba ya Yehova, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu.


pamodzi ndi iwo oyesedwa mwa chibadwidwe cha amuna, kuyambira a zaka zitatu ndi mphambu, kwa aliyense amene adalowa m'nyumba ya Yehova, monga mwa ntchito yake pa tsiku lake, kukachita za utumiki wao mu udikiro wao monga mwa zigawo zao;


Ichi ndi cha Alevi: kuyambira ali wa zaka makumi awiri ndi zisanu ndi mphambu azilowa kutumikira utumikiwu mu ntchito ya chihema chokomanako;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa