Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 23:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo anasonkhanitsa akulu onse a Israele, ndi ansembe ndi Alevi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo anasonkhanitsa akulu onse a Israele, ndi ansembe ndi Alevi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Davide adasonkhanitsa atsogoleri onse a Israele, ansembe ndi Alevi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye anasonkhanitsanso pamodzi atsogoleri onse a Israeli, pamodzi ndi ansembe ndi Alevi.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 23:2
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anafunsana ndi akulu a zikwi ndi a mazana, inde atsogoleri ali onse.


Atakalamba tsono Davide ndi kuchuluka masiku, iye analonga mwana wake Solomoni akhale mfumu ya Israele.


Ndipo anawerengedwa Alevi oyambira zaka makumi atatu ndi mphambu, ndipo chiwerengo chao kuwawerenga mmodzimmodzi ndicho amuna zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi zitatu.


Pamenepo Davide anasonkhanitsa ku Yerusalemu akalonga a Israele, akalonga a mafuko, ndi akulu a zigawo zakutumikira mfumu, ndi akulu a zikwi, ndi akulu a mazana, ndi akulu a zolemera zonse, ndi zoweta zonse za mfumu, ndi ana ake; pamodzi ndi akapitao ndi anthu amphamvu, ndiwo ngwazi zamphamvu onsewo.


Ndipo oimirirawo, ndi ana ao, ndi awa: a ana a Akohati, Hemani woimbayo, mwana wa Yowele, mwana wa Samuele,


Yoswa anaitana Aisraele onse, akuluakulu ao, ndi akulu ao, ndi oweruza ao, ndi akapitao ao, nanena nao, Ndakalamba, ndine wa zaka zambiri;


Ndipo Yoswa anasonkhanitsa mafuko onse a Israele ku Sekemu, naitana akuluakulu a Israele ndi akulu ao, ndi oweruza ao, ndi akapitao ao; ndipo anadzionetsa pamaso pa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa