1 Mbiri 21:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Davide anati kwa Yowabu ndi kwa akulu a anthu, Kawerengeni Israele kuyambira ku Beereseba kufikira ku Dani; nimundibwezere mau, kuti ndidziwe chiwerengo chao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Davide anati kwa Yowabu ndi kwa akulu a anthu, Kawerengeni Israele kuyambira ku Beereseba kufikira ku Dani; nimundibwezere mau, kuti ndidziwe chiwerengo chao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Choncho Davide adauza Yowabu mtsogoleri wa ankhondo kuti, “Pita, ukaŵerenge Aisraele kuyambira ku Beereseba mpaka ku Dani, ndipo udzandiwuze, kuti ndidziŵe chiŵerengero chao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Choncho Davide anati kwa Yowabu pamodzi ndi atsogoleri a ankhondo, “Pitani mukawerenge Aisraeli kuyambira ku Beeriseba mpaka ku Dani. Ndipo mudzandiwuze kuti ndidziwe chiwerengero chawo.” Onani mutuwo |