1 Mbiri 20:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo potonza Israele iyeyu Yonatani mwana wa Simea mbale wake wa Davide anamkantha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo potonza Israele iyeyu Yonatani mwana wa Simea mbale wake wa Davide anamkantha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsiku lina pamene adanyoza Aisraele, Yonatani, mwana wa Simea, mbale wake wa Davide, adamupha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pamene iye ankanyoza Aisraeli, Yonatani mwana wa Simea, mʼbale wake wa Davide anamupha. Onani mutuwo |