1 Mbiri 2:7 - Buku Lopatulika7 Ndi ana a Karimi: Akara wovuta Israeleyo, amene analakwira choperekedwa chiperekerecho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndi ana a Karimi: Akara wovuta Israeleyo, amene analakwira choperekedwa chiperekerecho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ana a Karimi naŵa: Akara amene adaavuta Aisraele. Iyeyo adaaba zinthu zoyenera kuziwononga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mwana wa Karimi anali Akani, amene anabweretsa mavuto pakati pa Israeli pamene anatenga zinthu zoyenera kuwonongedwa. Onani mutuwo |