Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 2:52 - Buku Lopatulika

52 Ndipo Sobala atate wa Kiriyati-Yearimu anali ndi ana: Harowe, ndi Hazi Amenuwoti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

52 Ndipo Sobala atate wa Kiriyati-Yearimu anali ndi ana: Harowe, ndi Hazi Amenuwoti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

52 Sobala bambo wake wa Kiriyati-Yearimu adaberekanso ana ena, naŵa: Harowe, ndiye kuti theka la Amenuwoti.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

52 Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi: Harowe, theka la banja la Manahati,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 2:52
5 Mawu Ofanana  

Salima atate wa Betelehemu, Harefi atate wa Betegadere.


Ndi mabanja a Kiriyati-Yearimu: Aitiri, ndi Aputi, ndi Asumati, ndi Amisrai; Azorati ndi Aestaoli anafuma kwa iwowa.


Ana a Salima: Betelehemu, ndi Anetofa, Ataroti-Beti-Yowabu, ndi Hazi Amanahati, ndi Azori.


Ndipo Reaya mwana wa Sobala anabala Yahati; ndi Yahati anabala Ahumai, ndi Lahadi. Iwo ndiwo mabanja a Azorati.


Ndipo ana a Israele anayenda ulendo, nafika kumizinda yao tsiku lachitatu. Koma mizinda yao ndiyo Gibiyoni, ndi Kefira, ndi Beeroti ndi Kiriyati-Yearimu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa