Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 2:5 - Buku Lopatulika

5 Ana a Perezi: Hezironi, ndi Hamuli.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ana a Perezi: Hezironi, ndi Hamuli.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ana a Perezi naŵa: Hezironi ndi Hamuli.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ana a Perezi anali awa: Hezironi ndi Hamuli.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 2:5
8 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Yuda: Eri, ndi Onani, ndi Sela, ndi Perezi, ndi Zera; koma Eri ndi Onani anafa m'dziko la Kanani. Ndi ana aamuna a Perezi ndiwo Hezironi ndi Hamuli.


Ndi Tamara mpongozi wake anambalira Perezi ndi Zera. Ana aamuna onse a Yuda ndiwo asanu.


Ndi ana a Zera: Zimiri, ndi Etani, ndi Hemani, ndi Kalikoli, ndi Dara; onse pamodzi ndi asanu.


Ana a Yuda: Perezi, Hezironi, ndi Karimi, ndi Huri, ndi Sobala.


Ndipo ana a Perezi ndiwo: Hezironi, ndiye kholo la banja la Ahezironi; Hamuli, ndiye kholo la banja la Ahamuli.


ndi Yuda anabala Perezi ndi Zera mwa Tamara; ndi Perezi anabala Hezironi; ndi Hezironi anabala Ramu;


mwana wa Aminadabu, mwana wa Admini, mwana wa Arini, mwana wa Hezironi, mwana wa Perezi, mwana wa Yuda,


Iyo ndiyo mibadwo ya Perezi; Perezi anabala Hezironi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa