Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 2:34 - Buku Lopatulika

34 Ndipo Sesani analibe ana aamuna, koma ana aakazi. Ndi Sesani anali naye mnyamata Mwejipito dzina lake ndiye Yara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Ndipo Sesani analibe ana amuna, koma ana akazi. Ndi Sesani anali naye mnyamata Mwejipito dzina lake ndiye Yara.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Sesani analibe ana aamuna, anali ndi ana aakazi okhaokha. Koma anali ndi kapolo wake wa ku Ejipito, dzina lake Yara.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha. Iye anali ndi wantchito wa ku Igupto, dzina lake Yariha.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 2:34
3 Mawu Ofanana  

Ndi mwana wa Apaimu: Isi. Ndi mwana wa Isi: Sesani. Ndi mwana wa Sesani: Alai.


Ndi ana a Yonatani: Peleti, ndi Zaza. Ndiwo ana a Yerameele.


Ndipo Sesani anampatsa Yara mnyamata wake mwana wake wamkazi akhale mkazi wake, ndipo anambalira Atai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa