Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 2:18 - Buku Lopatulika

18 Ndi Kalebe mwana wa Hezironi anabala ana ndi Azuba mkazi wake, ndi Yerioti; ndipo ana ake ndiwo Yesere, ndi Sobabu, ndi Aridoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndi Kalebe mwana wa Hezironi anabala ana ndi Azuba mkazi wake, ndi Yerioti; ndipo ana ake ndiwo Yesere, ndi Sobabu, ndi Aridoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Kalebe mwana wa Hezironi anali nawo ana omubalira mkazi wake Azuba ndiponso Yerioti. Ana amene adabala mkaziyo naŵa: Yesere, Sobabu ndi Aridoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 2:18
7 Mawu Ofanana  

Ndi Abigaile anabala Amasa; ndi atate wa Amasa ndiye Yetere Mwismaele.


Namwalira Azuba, ndi Kalebe anadzitengera Efurata, amene anambalira Huri.


Ndipo atafa Hezironi mu Kalebe-Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anambalira Asiriya atate wa Tekowa.


Ndi ana a Kalebe mbale wa Yerameele ndiwo Mesa mwana wake woyamba, ndiye atate wa Zifi; ndi ana a Maresa atate wa Hebroni.


Ndi Efa mkazi wamng'ono wa Kalebe anabala Harani, ndi Moza, ndi Gazezi; ndi Harani anabala Gazezi.


Ndi ana a Hezironi anambadwirawo: Yerameele, ndi Ramu, ndi Kalebe.


Ana a Yuda: Perezi, Hezironi, ndi Karimi, ndi Huri, ndi Sobala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa