1 Mbiri 2:16 - Buku Lopatulika16 ndi alongo ao ndiwo Zeruya ndi Abigaile. Ndi ana a Zeruya: Abisai ndi Yowabu, ndi Asahele; atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 ndi alongo ao ndiwo Zeruya ndi Abigaile. Ndi ana a Zeruya: Abisai ndi Yowabu, ndi Asahele; atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Alongo ao anali Zeruya ndi Abigaile. Ana a Zeruya naŵa: Abisai, Yowabu ndi Asahele, onse pamodzi atatu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli. Onani mutuwo |