Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 2:12 - Buku Lopatulika

12 ndi Bowazi anabala Obedi, ndi Obedi anabala Yese,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 ndi Bowazi anabala Obedi, ndi Obedi anabala Yese,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Bowazi adabereka Obede, Obede adabereka Yese.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 2:12
11 Mawu Ofanana  

osafunsira kwa Yehova; chifukwa chake anamupha, napambutsira ufumu kwa Davide mwana wa Yese.


ndi Nasoni anabala Salimoni, ndi Salimoni anabala Bowazi,


ndi Yese anabala mwana wake wamwamuna woyamba Eliyabu, ndi Abinadabu wachiwiri, ndi Simea wachitatu,


Ndipo padzatuluka mphukira pa tsinde la Yese, ndi nthambi yotuluka m'mizu yake idzabala zipatso;


Ndipo padzakhala tsiku lomwelo, kuti muzu wa Yese umene uima ngati mbendera ya mitundu ya anthu, amitundu adzafunafuna uwu; ndipo popuma pake padzakhala ulemerero.


ndi Salimoni anabala Bowazi mwa Rahabu; ndi Bowazi anabala Obede mwa Rute; ndi Obede anabala Yese;


mwana wa Yese, mwana wa Obede, mwana wa Bowazi, mwana wa Salimoni, mwana wa Nasoni,


Ndipo m'mene atamchotsa iye, anawautsira Davide akhale mfumu yao; amenenso anamchitira umboni, nati, Ndapeza Davide, mwana wa Yese, munthu wa pamtima panga, amene adzachita chifuniro changa chonse.


Ndiponso, Yesaya ati, Padzali muzu wa Yese, ndi Iye amene aukira kuchita ufumu pa anthu amitundu; Iyeyo anthu amitundu adzamuyembekezera.


ndi Obedi anabala Yese, ndi Yese anabala Davide.


Ndipo Yehova ananena ndi Samuele, Iwe ukuti ulire chifukwa cha Saulo nthawi yotani, popeza Ine ndinamkana kuti asakhale mfumu ya Israele? Dzaza nyanga yako ndi mafuta, numuke, ndidzakutumiza kwa Yese wa ku Betelehemu; pakuti ndinadzionera mfumu pakati pa ana ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa