1 Mbiri 18:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Davide anakantha Hadadezere mfumu ya Zoba ku Hamati, pomuka iye kukhazikitsa ulamuliro wake ku mtsinje wa Yufurate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Davide anakantha Hadadezere mfumu ya Zoba ku Hamati, pomuka iye kukhazikitsa ulamuliro wake ku mtsinje wa Yufurate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ku Hamati Davideyo adagonjetsanso Hadadezere mfumu ya ku Zoba, pamene inkapita kukakhazikitsa ulamuliro wake ku mtsinje wa Yufurate. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Komanso Davide anagonjetsa Hadadezeri mfumu ya Zoba, mpaka ku Hamati, pamene anapita kukakhazikitsa ulamuliro wake mʼmbali mwa mtsinje wa Yufurate. Onani mutuwo |