Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 17:4 - Buku Lopatulika

4 Kauze Davide mtumiki wanga, Atero Yehova, Usandimangire nyumba yokhalamo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Kauze Davide mtumiki wanga, Atero Yehova, Usandimangire nyumba yokhalamo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 “Kamuuze mtumiki wanga Davide kuti Ine Chauta ndikuti, Sudzandimangira ndiwe nyumba yoti ndizikhalamo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 “Pita kamuwuze mtumiki wanga Davide kuti, ‘Yehova akunena kuti, sudzandimangira ndiwe nyumba yokhalamo.’

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 17:4
8 Mawu Ofanana  

Koma usamange ndiwe nyumbayo, koma mwana wako adzatuluka m'chuuno mwako, iyeyo adzamangira dzina langa nyumba.


Ndipo usiku womwewo mau a Mulungu anadzera Natani, ndi kuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa