Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 17:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo usiku womwewo mau a Mulungu anadzera Natani, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo usiku womwewo mau a Mulungu anadzera Natani, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Koma usiku womwewo Chauta adauza Natani kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Usiku umenewo mawu a Mulungu anafika kwa Natani, ndipo anati,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 17:3
7 Mawu Ofanana  

Kuyambira tsiku lakutulutsa Ine anthu anga Aisraele m'dziko la Ejipito, sindinasankhe mzinda uliwonse mwa mafuko onse a Israele kumangamo nyumba yokhalamo dzina langa, koma ndinasankha Davide kukhala mfumu ya anthu anga Aisraele.


Ndipo Natani anati kwa Davide, Muchite zonse zili m'mtima mwanu; pakuti Mulungu ali nanu.


Kauze Davide mtumiki wanga, Atero Yehova, Usandimangire nyumba yokhalamo;


ndipo makutu ako adzamva mau kumbuyo kwa iwe akuti, Njira ndi iyi, yendani inu m'menemo: potembenukira inu kulamanja, ndi potembenukira kulamanzere.


Pakuti Ambuye Yehova sadzachita kanthu osawulula chinsinsi chake kwa atumiki ake aneneri.


Ndipo anati, Tamvani, tsono mau anga; pakakhala mneneri pakati pa inu, Ine Yehova ndidzizindikiritsa kwa iye m'masomphenya, ndinena naye m'kulota.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa