1 Mbiri 17:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Natani anati kwa Davide, Muchite zonse zili m'mtima mwanu; pakuti Mulungu ali nanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Natani anati kwa Davide, Muchite zonse zili m'mtima mwanu; pakuti Mulungu ali nanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Natani adauza Davide kuti, “Ai, chitani chilichonse chimene mukuganiza mumtima mwanu, poti Mulungu ali nanu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Natani anayankha Davide kuti, “Chitani chilichonse chimene chili mu mtima mwanu, chifukwa Mulungu ali nanu.” Onani mutuwo |