Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 16:9 - Buku Lopatulika

9 Muimbireni, muimbireni zomlemekeza; fotokozerani zodabwitsa zake zonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Muimbireni, muimbireni zomlemekeza; fotokozerani zodabwitsa zake zonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Imbirani Chauta, muimbireni nyimbo zomtamanda, lalikani za ntchito zake zodabwitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Imbirani Iye, muyimbireni nyimbo zamatamando; nenani za ntchito zake zonse zodabwitsa.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 16:9
16 Mawu Ofanana  

Mudzitamandire ndi dzina lake lopatulika; mitima yao ya iwo ofuna Yehova ikondwere.


Fotokozerani ulemerero wake mwa amitundu, zodabwitsa zake mwa mitundu yonse ya anthu.


Yamikani Yehova, itanani dzina lake; bukitsani mwa mitundu ya anthu zochita Iye.


Kumbukirani kuti mukuze ntchito zake zimene anaziimbira anthu.


Kudziwitsa ana a anthu zamphamvu zake, ndi ulemerero waukulu wa ufumu wake.


Chilungamo chanu sindinachibise m'kati mwamtima mwanga; chikhulupiriko chanu ndi chipulumutso chanu ndinachinena; chifundo chanu ndi choonadi chanu sindinachibisire msonkhano waukulu.


Mulungu, mwandiphunzitsa kuyambira ubwana wanga; ndipo kufikira lero ndilalikira zodabwitsa zanu.


Pamenepo iwo akuopa Yehova analankhulana wina ndi mnzake; ndipo Yehova anawatchera khutu namva, ndi buku la chikumbutso linalembedwa pamaso pake, la kwa iwo akuopa Yehova, nakumbukira dzina lake.


Ndipo pamene anaimba nyimbo, anatuluka kunka kuphiri la Azitona.


ndi kudzilankhulira nokha ndi masalimo, ndi mayamiko, ndi nyimbo zauzimu, kuimbira ndi kuimba m'malimba Ambuye mumtima mwanu;


Mau a Khristu akhalitse mwa inu chichulukire mu nzeru yonse, ndi kuphunzitsa ndi kuyambirirana eni okha ndi masalimo, ndi mayamiko ndi nyimbo zauzimu, ndi kuimbira Mulungu ndi chisomo mumtima mwanu.


Kodi wina wa inu akumva zowawa? Apemphere. Kodi wina asekera? Aimbire.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa