Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 15:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo Davide anasonkhanitsa ana a Aroni ndi Alevi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Davide anasonkhanitsa ana a Aroni ndi Alevi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono Davide adasonkhanitsa zidzukulu za Aroni ndi Alevi enanso.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Iye anayitanitsa pamodzi zidzukulu za Aaroni ndi Alevi:

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 15:4
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anati kwa msonkhano wonse wa Israele, Chikakomera inu, ndipo chikachokera kwa Yehova Mulungu wathu, titumize konse kuti abale athu otsala m'dziko lonse la Israele, ndi ansembe ndi Alevi okhala nao m'mizinda yao yokhala napo podyetsa, kuti asonkhane kwa ife;


a ana a Kohati, Uriyele mkulu wao, ndi abale ake zana limodzi mphambu makumi awiri;


Koma Nadabu ndi Abihu anafa pamaso pa Yehova muja anabwera nao moto wachilendo pamaso pa Yehova, m'chipululu cha Sinai, ndipo analibe ana; koma Eleazara ndi Itamara anachita ntchito ya nsembe pamaso pa atate wao Aroni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa