1 Mbiri 15:2 - Buku Lopatulika2 Pamenepo Davide anati, Sayenera ena kusenza likasa la Mulungu koma Alevi ndiwo; pakuti Yehova anawasankha iwo kusenza likasa la Mulungu, ndi kumtumikira Iye kosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pamenepo Davide anati, Sayenera ena kusenza likasa la Mulungu koma Alevi ndiwo; pakuti Yehova anawasankha iwo kusenza likasa la Mulungu, ndi kumtumikira Iye kosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono Davide adati, “Alevi okha ndiwo amene asenze Bokosi lachipangano la Mulungu, wina aliyense ai, pakuti Chauta adasankhula Aleviwo kuti azisenza Bokosilo ndiponso kuti azimtumikira mpaka muyaya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pamenepo Davide anati, “Palibe wina ati anyamule Bokosi la Mulungu koma Alevi chifukwa Yehova anawasankha kuti azinyamula Bokosi la Yehova ndi kumatumikira pamaso pake nthawi zonse.” Onani mutuwo |