1 Mbiri 15:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Davide anadzimangira nyumba m'mzinda mwake, nakonzeratu malo likasa la Mulungu, naliutsira hema. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Davide anadzimangira nyumba m'mudzi mwake, nakonzeratu malo likasa la Mulungu, naliutsira hema. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Davide adadzimangira nyumba zina mu mzinda wa Davide. Adakonza malo a Bokosi lachipangano la Chauta, namanga hema loikamo Bokosilo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Davide atadzimangira nyumba zina mu Mzinda wa Davide, iye anakonza malo a Bokosi la Mulungu ndipo analimangira tenti. Onani mutuwo |