1 Mbiri 13:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo pamene anafika ku dwale la Kidoni, Uza anatambasula dzanja lake kulichirikiza likasa, pakuti ng'ombe zikadapulumuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo pamene anafika ku dwale la Kidoni, Uza anatambasula dzanja lake kulichirikiza likasa, pakuti ng'ombe zikadapulumuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono atafika ku malo ophunthirapo tirigu ku Kidoni, ng'ombe zidaafuna kugwetsa Bokosi lija, ndiye Uza nkutambalitsa dzanja kuti aligwirire Bokosilo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Atafika pa malo opunthira tirigu ku Kidoni, Uza anatambalitsa dzanja lake kuti agwire bokosilo, chifukwa ngʼombe zinkafuna kugwa. Onani mutuwo |