1 Mbiri 13:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anatengera likasa la Mulungu pa galeta watsopano kuchokera kunyumba ya Abinadabu; ndi Uza ndi Ahiyo anayendetsa ng'ombe za pa galetayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anatengera likasa la Mulungu pa galeta watsopano kuchokera kunyumba ya Abinadabu; ndi Uza ndi Ahiyo anayendetsa ng'ombe za pa galetayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Bokosi lachipanganolo adalinyamula pa ngolo yatsopano, kuchoka nalo ku nyumba ya Abinadabu. Uza ndi Ahiyo ndiwo amene ankayendetsa ngoloyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iwo anachotsa Bokosi la Mulungu ku nyumba ya Abinadabu pa ngolo yatsopano. Uza ndi Ahiyo ndiwo ankayendetsa ngoloyo. Onani mutuwo |