1 Mbiri 13:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Davide ndi Aisraele onse pamodzi naye anakwera kunka ku Baala, ndiko ku Kiriyati-Yearimu wa mu Yuda, kukwera nalo kuchokera komweko likasa la Mulungu Yehova wakukhala pa akerubi, kumene aitanirako Dzina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Davide ndi Aisraele onse pamodzi naye anakwera kunka ku Baala, ndiko ku Kiriyati-Yearimu wa m'Yuda, kukwera nalo kuchokera komweko likasa la Mulungu Yehova wakukhala pa akerubi, kumene aitanirako Dzina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo Davide pamodzi ndi Aisraele onse adakwera kupita ku Baala, ndiye kuti ku Kiriyati-Yearimu m'dera la ku Yuda, kuti akatenge Bokosi lachipangano la Mulungu. Bokosilo limadziŵika ndi dzina la Chauta amene amakhala pa akerubi ngati pa mpando waufumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Davide pamodzi ndi Aisraeli onse anapita ku Baalahi (Kiriati-Yearimu) ku Yuda kukatenga Bokosi la Yehova Mulungu, amene amakhala pakati pa akerubi. Limeneli ndiye Bokosi la Chipangano lomwe limadziwika ndi Dzina lake. Onani mutuwo |