1 Mbiri 13:5 - Buku Lopatulika5 M'mwemo Davide anamemeza Aisraele onse kuyambira Sihori wa ku Ejipito mpaka polowera ku Hamati, kutenga likasa la Mulungu ku Kiriyati-Yearimu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 M'mwemo Davide anamemeza Aisraele onse kuyambira Sihori wa ku Ejipito mpaka polowera ku Hamati, kutenga likasa la Mulungu ku Kiriyati-Yearimu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Choncho Davide adasonkhanitsa Aisraele onse kuyambira ku mtsinje wa Sihori ku Ejipito mpaka ku chipata cha Hamati, kuti abwere nalo Bokosi lachipangano la Mulungu kuchokera ku Kiriyati-Yearimu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kotero Davide anasonkhanitsa Aisraeli onse, kuchokera ku mtsinje wa Sihori ku Igupto mpaka ku Lebo Hamati, kuti abweretse Bokosi la Mulungu kuchokera ku Kiriati-Yearimu. Onani mutuwo |