1 Mbiri 13:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo a msonkhano onse anati kuti adzachita; pakuti chidayenera chinthuchi pamaso pa anthu onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo a msonkhano onse anati kuti adzachita; pakuti chidayenera chinthuchi pamaso pa anthu onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Msonkhano wonse udavomereza zimenezo, poti anthu onse adaaona kuti nzabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Gulu lonse linavomereza izi, pakuti anthu onse anaona kuti kunali kofunika kutero. Onani mutuwo |