1 Mbiri 13:13 - Buku Lopatulika13 M'mwemo Davide sanafike nalo likasa kwao kumzinda wa Davide, koma analipambutsira kunyumba ya Obededomu wa ku Giti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 M'mwemo Davide sanafike nalo likasa kwao kumudzi wa Davide, koma analipambutsira kunyumba ya Obededomu wa ku Giti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Motero sadabwere nalo Bokosilo kwao ku mzinda wa Davide, koma adalipatutsira ku nyumba ya Obededomu Mgiti. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Iye sanapitenso nalo Bokosi la Mulungu ku Mzinda wa Davide. Mʼmalo mwake anapita nalo ku nyumba ya Obedi-Edomu Mgiti. Onani mutuwo |