1 Mbiri 13:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Davide anaopa Mulungu tsikulo, kuti, Ndidzafika nalo bwanji likasa la Mulungu kwathu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Davide anaopa Mulungu tsikulo, kuti, Ndidzafika nalo bwanji likasa la Mulungu kwathu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Davide adachita mantha ndi Mulungu tsiku limenelo, ndipo adafunsa kuti, “Kodi ndingathe bwanji kufika nalo kwathu Bokosi la Mulunguli?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tsiku limenelo Davide anachita mantha ndi Mulungu ndipo anafunsa kuti, “Kodi Bokosi la Mulungu lingafike bwanji kwathu?” Onani mutuwo |