1 Mbiri 13:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo kudaipira Davide kuti Yehova adachita chipasulo ndi Uza; motero anatcha malowo Pereziuza, mpaka lero lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo kudaipira Davide kuti Yehova adachita chipasulo ndi Uza; motero anatcha malowo Pereziuza, mpaka lero lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono Davide adakhumudwa chifukwa chakuti Chauta adaakantha Uza. Ndipo mpaka pano malo amenewo amaŵatchula kuti Pereziuza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndipo Davide anakhumudwa chifukwa Yehova anakantha Uza ndipo mpaka lero malowo amatchedwa Perezi Uza. Onani mutuwo |