1 Mbiri 11:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Davide anakulakulabe, pakuti Yehova wa makamu anali naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Davide anakulakulabe, pakuti Yehova wa makamu anali naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Motero mphamvu za Davide zidanka zikulirakulira, chifukwa Chauta wamphamvuzonse anali naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo mphamvu za Davide zinkakulirakulira chifukwa anali ndi Yehova Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |