1 Mbiri 11:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Davide anakhala m'lingamo; chifukwa chake analitcha mzinda wa Davide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Davide anakhala m'lingamo; chifukwa chake analitcha mudzi wa Davide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Popeza kuti Davide ankakhala m'lingamo, lingalo linkatchedwa Mzinda wa Davide. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tsono Davide anakhazikika mu lingamo, ndipo mzindawu anawutcha Mzinda wa Davide. Onani mutuwo |