1 Mbiri 11:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo nzika za mu Yebusi zinati kwa Davide, Sungalowe muno. Koma Davide analanda linga la Ziyoni, ndiwo mzinda wa Davide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo nzika za m'Yebusi zinati kwa Davide, Sungalowe muno. Koma Davide analanda linga la Ziyoni, ndiwo mudzi wa Davide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ayebusiwo adauza Davide kuti, “Kuno sudzaloŵako ai.” Komabe Davideyo adalanda linga la Ziyoni, ndiye kuti Mzinda wa Davide. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 anamuwuza Davide kuti, “Simulowa muno.” Komabe Davide analanda linga la Ziyoni, limene ndi mzinda wa Davide. Onani mutuwo |